National Anthems & Patriotic Songs "Malawian National Anthem - Mulungu dalitsa Malaŵi" lyrics

Translation to:enptruto

Malawian National Anthem - Mulungu dalitsa Malaŵi

Mlungu dalitsani Malaŵi,Mumsunge m'mtendere.Gonjetsani adani onse,Njala, nthenda, nsanje.Lunzitsani mitima yathu,Kuti tisaope.Mdalitse Mtsogoleri nafe,Ndi Mayi Malaŵi.

Malaŵi ndziko lokongola,La chonde ndi ufulu,Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri,Ndithudi tadala.Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,N'mphatso zaulere.Nkhalango, madambo abwino.Ngwokoma Malaŵi.

O Ufulu tigwirizane,Kukweza Malaŵi.Ndi chikondi, khama, kumvera,Timutumikire.Pa nkhondo nkana pa mtendere,Cholinga n'chimodzi.Mayi, bambo, tidzipereke,Pokweza Malaŵi.

Malawian National Anthem - O God bless our land of Malawi

O God bless our land of Malawi,Keep it a land of peace.Put down each and every enemy,Hunger, disease, envy.Join together all our hearts as one,That we be free from fear.Bless our leader, each and every one,And Mother Malawi.

Our own Malawi, this land so fair,Fertile and brave and free.With its lakes, refreshing mountain air,How greatly blest are we.Hills and valleys, soil so rich and rareGive us a bounty free.Wood and forest, plains so broad and fair,All - beauteous Malawi.

Freedom ever, let us all uniteTo build up Malawi.With our love, our zeal and loyalty,Bringing our best to her.In time of war, or in time of peace,One purpose and one goal.Men and women serving selflesslyIn building Malawi.

Here one can find the English lyrics of the song Malawian National Anthem - Mulungu dalitsa Malaŵi by National Anthems & Patriotic Songs. Or Malawian National Anthem - Mulungu dalitsa Malaŵi poem lyrics. National Anthems & Patriotic Songs Malawian National Anthem - Mulungu dalitsa Malaŵi text in English. This page also contains a translation, and Malawian National Anthem - Mulungu dalitsa Malaŵi meaning.